Amalifalensi Agha mu Ubumi Bwitu Ubwachikilisitu nu Bulumbilili Akabuku aka Nkomano
© 2023 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
MALICHI 4-10
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 16–17
“U Yehova, Chiziba Chane Icha Vintu Ivyiza”
w18.12-TB 26 ¶11
Ŵawukirano, Mungaŵa na Umoyo Wakukhorweska
ŴANI NA ŴABWEZI ŴAWEMI
11 Ŵazgani Salimo 16:3. Davide wakamanya umo wangasangira ŵabwezi ŵawemi. Wakasanga ŵabwezi ‘ŵakumukondweska chomene’ awo ŵakatemwanga Yehova. Wakayowoya kuti ŵakaŵa “ŵatuŵa” chifukwa ŵakaŵa na nkharo yiwemi. Wamasalimo munyake nayo wakajipulika nthena pakuyowoya za ŵabwezi awo wakasankha. Wakalemba kuti: “Nili mubwezi wa wose awo ŵakumopani, na awo ŵakusunga malanguro ghinu.” (Sal. 119:63) Nga umo tikawonera mu nkhani iyo yajumpha, namwe mungasanga ŵabwezi ŵawemi pakati pa ŵanthu awo ŵakopa Yehova na kumupulikira. Ndipo ŵabwezi aŵa ŵangaŵa ŵa vyaka vyakupambanapambana.
w14-TB 2/15 29 ¶4
‘Daŵirani Utozi wa Yehova’
“Yehova ndiye ciharo cane na nkhombo yane; ndimwe mukukhozga nkharo yane. Vyose vyandiwira mu malo gha cimwemwe.” (Sal. 16:5, 6) Davide wakawonganga “ciharo” cake ico nkhuŵa paubwezi na Yehova kweniso mwaŵi wa kumuteŵetera. Nga ni Davide, tingakumana na masuzgo, kweni tikutumbikika comene mwauzimu. Ntheura, mphanyi talutilira kukondwa na kusopa kwaunenesko ndipo nyengo zose ‘titataŵenge’ tempile lauzimu la Yehova na mtima wa kuwonga.
w08-TB 2/15 3 ¶2-3
Nyengo Zose Ŵikani Yehova Pamaso Pinu
2 Waliyose wa ise wangasambira vinandi kufuma ku ivyo vikacitikira ŵanthu ŵakumanyikwa makora awo Baibolo likuyowoya, nga ni Abrahamu, Sara, Mozesi, Rute, Davide, Esitere, mpositole Paulosi, na ŵanyake ŵantheura. Kweni nkhani za ŵanthu ŵanyake awo mbakumanyikwa viŵi yayi nazo zingatovwira. Kughanaghanira pa nkhani za mu Baibolo kungatovwira kuti ticitenge vinthu mwakuyana na mazgu gha wamasalmo agho ghakuti: “Nkhuŵika Yehova pamaso pane zuŵa na zuŵa; cifukwa Iye wali ku woko lane la [malyero] ine ntha ndisunkhunikenge.” (Sal. 16:8) Kasi mazgu agha ghakung’anamuraci?
3 Kale, panyengo ya nkhondo msilikari wakakoleranga lupanga ku woko la malyero, ico cikapangiskanga kuti cigaŵa ca woko ili ciŵe cambura kuvikilirika na ciskango ico cikaŵanga ku woko la mazere. Kweni wakaŵanga wakuvikilirika usange munyake wali pafupi na woko lake la malyero. Usange tikuŵika Yehova mu maghanoghano ghithu na kucita khumbo lake, wativikilirenge. Sono tiyeni tiwone umo kusanda nkhani za mu Baibolo kungakhozgera cipulikano cithu mwakuti ‘tiŵikenge Yehova pamaso pithu zuŵa na zuŵa.’
Vyo Twamanyila
it-2-E 714
Akamboni
Ilizyu ilya Chihebeli ilyakuti ʼi·shohnʹ (Kumbu. 32.10; Mbupi. 7.2), nanti balibombozya poka ni lizyu ilyakuti ʽaʹyin (ilyiso), likung’anamula ‘umwana umunyamata uwa lyiso’; umwakuyana bulo ilizyu ilyakuti bath (umwana umulindu) lyo babombezizye pa Inguto 2.18 likung’anamula ‘umwana umulindu uwa lyiso,’ ifundo zyosi zibili zikung’anamula akamboni ka lyiso. Pa simbo ilya Salimo 17.8 amazina ghabili agha bonganizye poka ukuti ifundo iyikulu yimanyikwe (ʼi·shohnʹ bath-ʽaʹyin),vyo vikung’anamula, ‘umwana umunyamata, umwana umulindu uwa lyiso’ (“akamboni ka lyiso,” NW). Ilifalesi ili likulangizya akachituzi akadono ko kakubonekelasona mwilyiso ilyamwabo.
Ilyiso, chigaba chimo cho chakulondiwa sana sona chikumanya lubilo waghe chimo chapalamasya papo napo kangaba kantu kadono ngati akasisi pamo akalusesenga. Akachipapa ko kakufighilila akamboni kope kabaghiye ukuba kakufighililiwa chifukwa nanti kangakomanika ichifukwa cha mbina vingapangisya ukuti ilyiso lileke ukwennya pamo ukufobela. Ukuyana na mo Ibayibolo likulongosolela likuti ‘akamboni kilyiso’ kakulondiwa ukufighililiwa nkani. Indaghilo zya Chala zyope momo zikulondiwa ukufighililiwa. (Mbupi. 7.2) Pakunena izya mo u tata u Chala akafighililagha Abaizilayeli, pi simbo ilya Ukukumbusya Indaghilo 32.10 likunena ukuti Akabafighilila ‘ngati kamboni kilyiso.’ U Devedi akalaba kwa Chala ukuti amufighilile nu kumupwelelela ngati ‘yo mboni yilyiso.’ (Sali. 17.8) Akalondagha ukuti u Yehova abombe mwalubilo pakumufighilila ku balwani bache. (Yanisya nu Zeka. 2.8; po babombezizye ilizyu ilya Chihebeli ilyakuti ba·vathʹ ʽaʹyin, ilyiso.)—Ennya po batili EYE.
MALICHI 11-17
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 18
“U Yehova Weyo Akumpoka Une”
w09-CN 5/1 14 ¶4-5
Kodi Mafanizo a M’Baibulo Mumawamvetsa Bwino?
Baibulo limayerekezeranso Yehova ndi zinthu zina zopanda moyo. Mwachitsanzo, limati iye ndi “Thanthwe la Isiraeli,” “thanthwe,” ndiponso “linga.” (2 Samueli 23:3; Salmo 18:2; Deuteronomo 32:4) Kodi zinthu zimenezi zikufanana bwanji ndi Yehova? Monga mmene thanthwe lilili lolimba ndiponso losasunthika, Yehova Mulungu ndiye chitetezo chathu cholimba ndiponso chosasunthika.
5 M’buku la Masalmo muli mafanizo ambiri amene amalongosola makhalidwe osiyanasiyana a Yehova. Mwachitsanzo, Salmo 84:11 limanena kuti Yehova ali ngati “dzuwa ndi chikopa,” chifukwa chakuti iye amatipatsa kuunika, moyo, mphamvu ndiponso amatiteteza. Komanso, Salmo 121:5 limati “Yehova ndiye mthunzi wako wa ku dzanja lako lamanja.” Anthu amene amam’tumikira, Yehova amawateteza ku mavuto otentha kwambiri ngati dzuwa, mofanana ndi mmene mthunzi umatetezera munthu kuti asapse ndi dzuwa. Amachita zimenezi powaphimba ndi mthunzi wa “dzanja” lake kapena wa “mapiko” ake.—Yesaya 51:16; Salmo 17:8; 36:7.
it-2-E 1161 ¶7
Inyiputo
U Chala akwivwa inyiputo izya babombi bache. Bo bakumubombela u Chala mu muzimu na mubwanaloli bakuba nu lusubilo losi ukuti akwivwa inyiputo zyabo napo bangamwiputa mu chinenelo chilichosi. Napo mungiputa ukusita ukufumya amazyu, u Chala ‘akwivwa’ sona akumanya ivya mu moyo wa muntu. (Sali. 66.19; 86.6; 116.1; 1 Samu. 1.13; Nehe. 2.4) U Chala akubivwa abantu bo bakumulilila po batamiwa, akwivwa inyiputo zyabo sona akumanya ichakulinga icha bantu abakususya bo bakulonda ukubabombela ivibibi ababombi bache.—Ubwa. 21.17; Sali. 55.18, 19; 69.33; 94.9-11; Yere. 23.25.
w22.04-TB 3 ¶1
Ivyo Tingachita Kuti Tizizipizge Para Tikwenjerwa
2. Ghanaghaniranipo. Para mukughanaghanira ivyo muli kujumphamo kumasinda, kasi vilipo viyezgo ivyo mukuwona kuti mukakwaniska kuzizipizga chifukwa cha wovwiri wa Yehova? Para tikughanaghanira umo Yehova wali kutovwilirapo ise kweniso ŵateŵeti ŵake ŵakumasinda, nkhongono zikukwera ndipo tikumugomezga chomene. (Sal. 18:17-19) Mulara munyake zina lake Joshua wakuti: “Nili kulemba malurombo agho ghali kuzgoreka. Ivi vikunovwira kuti nikumbukenge nyengo izo nkhapempha Yehova chinthu chinyake ndipo wakanipa icho nkhakhumbikwiranga.” Nadi, para tikughanaghanirapo pa ivyo Yehova wali kutichitirapo kale kumasinda, tikusanga nkhongono izo zingatovwira kuzizipizga para tikwenjerwa.
Vyo Twamanyila
it-1-E 432 ¶2
Kelubi
Abantumi aba batakapangiwa ngati bantumi bo abantu bo bakiputagha ivifwani bakababombezyanga pakwiputa ukwabumyasi, bo bakabonekagha bakoghofya ngati mo inkani zimo zikunenela. Ukuyana na mabukaboni gho Abayuda abakale bakalongosolagha (Ibayibolo litanenite nachimo pankani iyi), bakanena ukuti abakelubi aba bakaba na kabonekele ngati ka bantu. Abakelubi aba bakapangiwa akiza nkani, bakimilagha abantumi bo vipeliwa ivyakuyemba, sona bakapangiwa ‘umwakukonka ipulani’ yo u Mozesi akapokela ukufuma kwa Yehova. (Kuso. 25.9) Umutumiwa u Pabuli akabalongosola ukuti ‘abakelubi aba bakalangizyanga ubuchindamu ubwa Chala.’ (Hebe. 9.5) Abakelubi aba bakimilagha ukubapo kwa Yehova: ‘Une nkwiza pakubonekela kukwako sona nkwiza pakunena nuwe ukufuma pamwanya pa chikupikizyo, ukufuma pakasi pa bakelubi babili bo bali pamwanya pa bokosi ilya lufingo.’ (Kuso. 25.22; Kuba. 7.89) Polelo u Yehova akunena ukuti ‘ikaye pakasi pa bakelubi.’ (1 Samu. 4.4; 2 Samu. 6.2; 2 Nyafya. 19.15; 1 Syambu. 13.6; Sali. 80.1; 99.1; Yesa. 37.16) Abakelubi aba ‘bakwimila ingolo’ ya Yehova yo akwendesya (1 Syambu. 28.18), sona amapapindo agha bakerubi ghakubomba imbombo iya kufighilila po likuchimbila ni sipidi. Mu lwimbo lo u Devedi akimba akalongosola mo u Yehova akachimbilila pakwiza pakumwavwa ngati muntu yo ‘akwelite pa bakelubi sona pakwiza akubuluka’ na ‘mapapindo agha muzimu.’—2 Samu. 22.11; Sali. 18.10.
MALICHI 18-24
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 19–21
“Kumwanya Kukulumbilila Ubuchindamu bwa Chala”
w04-CN 1/1 8 ¶1-2
Anthu Onse Alengeze Ulemerero wa Yehova
DAVIDE, mwana wa Jese, anakula monga mbusa ku dera la ku Betelehemu. Ayenera kuti nthaŵi zambiri ankayang’anitsitsa kumwamba kodzaza ndi nyenyezi zambirimbiri usiku, kunja kuli zii, akuyang’anira ziweto za atate wake m’malo odyetserako nkhosa amene ankakhala kwaokha. Mosakayikira, anakumbukira zinthu zosaiŵalika zimenezi pamene, motsogozedwa ndi mzimu woyera wa Mulungu, analemba ndi kuyimba mawu ochititsa chidwi a mu Salmo 19, amene amati: “Zakumwamba zimalalikira ulemerero wa Mulungu; ndipo thambo lionetsa ntchito ya manja ake. Muyeso wawo wapitirira pa dziko lonse lapansi, ndipo mawu awo ku malekezero a m’dziko muli anthu.”—Salmo 19:1, 4.
2 Zakumwamba zochititsa chidwi zolengedwa ndi Yehova zimalengeza ulemerero wa Yehova usana ndi usiku popanda kulankhula, popanda mawu, popanda liwu lawo kumveka. Chilengedwe sichisiya kulengeza ulemerero wa Mulungu, ndipo tikaganizira kuti umboni wopanda mawu umenewu umapita “pa dziko lonse lapansi” kuti anthu onse okhalamo awuone, zimatichititsa kuzindikira kuti ndife ochepa mphamvu kwambiri. Komabe, umboni wopanda mawu wa chilengedwe si wokwanira. Anthu okhulupirika akulimbikitsidwa kulengeza nawo umboni umenewu ndi mawu awo. Wolemba salmo wina, amene dzina lake silinatchulidwe, anauza olambira okhulupirika kuti: “M’patseni Yehova ulemerero ndi mphamvu. M’patseni Yehova ulemerero wa dzina lake.” (Salmo 96:7, 8) Anthu amene ali ndi ubwenzi wabwino ndi Yehova amasangalala kumvera langizo limeneli. Koma kodi kupatsa Mulungu ulemerero kumatanthauza chiyani?
w04-CN 6/1 11 ¶8-10
Chilengedwe Chimalengeza Ulemerero wa Mulungu
8 Kenako, Davide anafotokoza chinthu china chodabwitsa m’chilengedwe cha Yehova. Anati: “Iye anaika hema la dzuŵa mmenemo [m’mwamba], ndipo lili ngati mkwati wakutuluka m’chipinda mwake, likondwera ngati chimphona kuthamanga m’njira. Kutuluka kwake lituluka kolekezera thambo, ndipo kuzungulira kwake lifikira kumalekezero ake: ndipo kulibe kanthu kobisalira kutentha kwake.”—Salmo 19:4-6.
9 Dzuŵa ndi locheperapo poyerekezera ndi nyenyezi zina. Komabe, ndi nyenyezi yaikulu, moti mapulaneti amene amazungulira dzuŵalo amaoneka aang’ono kwambiri. Buku lina limanena kuti dzuŵa ndi lolemera matani 2 biliyoni, biliyoni, biliyoni. Kulemera kumeneku kumaposeratu kutalitali kulemera kwa mapulaneti onse amene amazungulira dzuŵa kuwaphatikiza pamodzi. Mphamvu ya dzuŵa imachititsa kuti dziko lapansili lizizungulira dzuŵalo pa mtunda wa makilomita 150 miliyoni popanda kupatuka n’kupita kutali kapena kukokeka n’kuliyandikira kwambiri. Ndi mphamvu yochepa chabe ya dzuŵa imene imafika padziko lapansi koma ndi yokwanira kuti zamoyo zikhalepobe padzikoli.
10 Wamasalmo anagwiritsa ntchito mawu okuluŵika pofotokoza za dzuŵa pamene ananena kuti dzuŵa ndi “chimphona” chimene chimathamanga kuchokera kumalekezero ena kufika malekezero ena masana, ndipo usiku chimakagona mu “hema.” Nyenyezi yaikulu imeneyi ikamaloŵa kumadzulo, munthu akamaiona ali padziko lapansi imaoneka ngati imapita mu “hema,” ngati kuti ikukapuma. Kum’maŵa imaoneka ngati ikutumphuka, n’kuwala kwambiri “ngati mkwati wakutuluka m’chipinda mwake.” Popeza anali mbusa, Davide ankadziŵa kuti usiku kunali kuzizira kwambiri. (Genesis 31:40) Anali kukumbukira kuti dzuŵa linkamuchititsa kumva kutenthera mofulumira komanso kutenthetsa malo amene iye anali. Mwachionekere, silinali kutopa pa “ulendo” wake wochoka kum’maŵa kufika kumadzulo koma linali ngati “chimphona,” chokonzeka kubwerezanso ulendo wake.
g95-CN 11/8 7 ¶3
Waluso wonyalanyazidwa koposa m’Nthaŵi Yathu
Kukulitsa chiyamikiro chathu kaamba ka luso m’chilengedwe kungatithandize kudziŵa Mlengi wathu, amene ntchito zake zatizinga. Nthaŵi ina Yesu anauza ophunzira ake kuyang’anitsitsa maluŵa a mthengo omera m’Galileya. “Tapenyetsani maluŵa akuthengo,” iye anatero, “makulidwe awo; sagwiritsa ntchito kapena sapota; koma ndinena kwa inu, kuti angakhale Solomo mu ulemerero wake wonse sanavala monga limodzi la ameneŵa.” (Mateyu 6:28, 29) Kukongola kwa duŵa laling’ono kungatikumbutse kuti Mulungu sali wosasamala zofuna za banja la munthu.
Vyo Twamanyila
it-1-E 1073
Umuhebeli, II
Pali akasimbile kamo aka mazyu ko kakulongosola isentesi umwakupambanisya umwakuti isentesi iya bubili yikunena ivintu vyo vikupambanako ni sentesi iya bwandilo, loli isentesi iya bubili yikudidimizya ifundo iya mu sentesi iya bwandilo. Umwakufwanikizya pa Salimo 19.7-9 pali ichifwanikizyo icha kasimbile aka:
Indaghilo zya Yehova zyakufikapo,
zikunyosezyapo ubumi.
Ivikumbusyo vya Yehova visubaliwa,
vikumupangisya umupunganu ukuba wamahala.
Indaghilo zya Yehova zigholosu,
zikuhobosya umoyo;
Indaghilo zya Yehova zizelu,
zikuswefya amaso.
Ukoghopa u Yehova buzelu,
bukubapo bwila na bwila.
Ubulongi bwa Yehova bwa bwanaloli
sona bugholosu.
Mungennya ukuti ichigaba icha bubili icha sentesi chikumalizya ukulongosola ifundo iya vesi lyosi, po akasimbile aka mazyu aka kakupangisya ukuti twaghe ifundo yo yikwivwika ukufuma mu masentesi ghosi ghabili. Ichigaba ichabubili ngati ichakuti “zikunyosezyapo ubumi” sona “vikumupangisya umupunganu ukuba wamahala,” vikumwavwa yo akubelenga ukwennya mo ‘indaghilo zya Yehova zya kufikapo’ sona na mo “ivikumbusyo vya Yehova visubaliwa.” Akabalilo akinji akasimbile akakupambanisya aka, pa sentesi iyabwandilo ni yabubili kakudumula amazyu. Ukuti ifundo yibukilile pa kumanyikwa mu mavesi, bakuyisimba umwakupambanisya. Ichi cho chifukwa cho akasimbile aka kakwitiziwa ukuti formal or constructive parallelism.
MALICHI 25-31
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 22
Ibayibolo Likanenela Zila Ivyakukwafyannya Nimfwa ya Yesu
w11-TB 8/15 15 ¶16
Ŵakasanga Mesiya
16 Ucimi ukati vizamuwoneka nga Ciuta wamujowora Mesiya. (Ŵazgani Salmo 22:1.) Mwakuyana na ucimi uwu, “pa ora lacinkhondi na cinayi, [ca m’ma 3 koloko muhanya] Yesu wakacemerezga na lizgu likuru, wakati: ‘Eli Eli lama sabakatani?’ ico cikung’anamura kuti, ‘Ciuta wane, Ciuta wane, kasi mwanisidiraci?’” (Mrk. 15:34) Yesu wakaŵavya cipulikano mwa Ŵawiske yayi. Ciuta wakasida Yesu mu mawoko gha ŵalwani mwakuti wayezgeke mwakukwana. Ndipo apo wakaliranga, Yesu wakafiskanga ucimi uwo wuli pa Salmo 22:1.
w11-TB 8/15 15 ¶13
Ŵakasanga Mesiya
13 Davide wakacima kuti Mesiya wazamuneneka. (Ŵazgani Salmo 22:7, 8.) Yesu wakatukika apo wakatambuzgikanga pa khuni lakusuzgikirapo. Mateyu wakati: “Ŵanthu awo ŵakajumphanga ŵakamba kumunena, kupukunya mitu yawo ndipo ŵakati: ‘Iwe, wamweneiwe ukatenge uwiskirenge pasi tempele na kulizenga mu mazuŵa ghatatu, jiponoska wamwene! Usange ndiwe mwana wa Ciuta, khira pa khuni lakusuzgikirapo!’” Kweniso ŵalara ŵa ŵasofi, ŵalembi, na ŵanalume ŵalara nawo ŵakamba kumuhoya ndipo ŵakati: “Wakaponoska ŵanyake; iyomwene wangajiponoska cara! Iyo ni Themba la Israyeli; sono lekani wakhire pa khuni lakusuzgikirapo ndipo timugomezgenge. Iyo waŵika cigomezgo cake mwa Ciuta; usange Ciuta wakukondwa nayo, ipo wamuthaske, cifukwa wakati, ‘Nili Mwana wa Ciuta.’” (Mat. 27:39-43) Kweni Yesu wakazizipizga vyose ivi, ndipo nchakuwonerapo ciwemi comene kwa ise.
w11-TB 8/15 15 ¶14
Ŵakasanga Mesiya
14 Ucimi ukati ŵamucita mayere pa vyakuvwara vya Mesiya. Wamasalimo wakati: “Ŵakugaŵana vyakuvwara vyane, munjilira wane ŵakuwupenduzgira.” (Sal. 22:18) Ici ndico nadi cikacitika, “ŵakati ŵamupayika [ŵasilikari Ŵaciroma] ŵakagaŵa malaya ghake ghakuwaro mwa kupenduzga.”—Mat. 27:35; ŵazgani Yohane 19:23, 24.
Vyo Twamanyila
w06-TB 11/1 29 ¶7
Kucindika Maungano Ghithu Ghakupatulika
7 Pali nthowa izo tingacindikira maungano ghithu. Nthowa yimoza ndiyo kuŵapo pakwimba sumu za Ufumu. Sumu zinandi zili kulembeka nga malurombo ndipo zikwenera kwimbika mwanchindi. Pakuzunura mazgu gha mu Salmo 22, mpositole Paulosi wakalemba za Yesu kuti: “Nditi ndithuwuske zina linu ku ŵabali ŵane, Mukati mu ekleziya nditi ndimutamikani na lusumu.” (Ŵahebere 2:12) Ntheura, tikwenera kuyezgayezga kuti tiŵengepo para ceyamani wakwambiska sumu na kughanaghanira ivyo mazgu gha mu sumu ghakung’anamura para tikwimba. Kimbiro kithu mphanyi kalongora umo wakajipulikira wamasalmo uyo wakalemba kuti: “Tindimuwonge Yehova na mtima wane wose, mu wupu wa ŵakunyoroka, na mu ungano.” (Salmo 111:1) Inya, kwimbira Yehova malumbo nchifukwa ciwemi cakufikira luŵiro pa maungano na kuŵapo mpaka paumaliro.
w03-CN 9/1 20 ¶1
Tamandani Yehova “Pakati pa Msonkhano”
Masiku ano, monga mmene zinthu zinalili kale, anthu okhulupirira amapatsidwa mwayi woti azitha kulankhula za chikhulupiriro chawo “pakati pa msonkhano.” Aliyense ali ndi mwayi woyankha mafunso amene amafunsidwa kwa omvetsera pa misonkhano ya mpingo. Musamapeputse mphamvu ya ndemanga zimenezi. Mwachitsanzo, ndemanga zimene zimasonyeza zimene tingachite kuti tithane ndi mavuto kapena tiwapeŵe zimalimbikitsa abale kuti apitirizebe kutsatira mfundo za m’Baibulo. Ndemanga zofotokoza malemba a m’Baibulo amene atchulidwa koma sanawagwire mawu pandimepo, kapena zofotokoza mfundo zimene munthu wapeza atachita kafukufuku payekha, zingalimbikitse ena kukulitsa chizoloŵezi chophunzira paokha.
EPULELO 1-7
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 23–25
“U Yehova Mudimi Wane”
w11-TB 5/1 31 ¶3
“Yehova Ndiye Muliska Wane”
Yehova wakulongozga mberere zake. Para mberere zilije muliska zikuzgeŵa. Mwakuyana waka, nase tikwenera kovwirika kuti tende mu nthowa ya umoyo. (Yeremiya 10:23) Davide wakalongosora kuti, Yehova wakulongozgera ŵanthu ŵake ku “maluhari ghakuteketera” ndiposo “ku maji ghakudama.” Wakuŵalongozgera “mu nthowa za urunji.” (Mavesi 2, 3) Mazgu ghakuyelezgera agha ghakutisimikizgira kuti tikwenera kugomezga Ciuta. Para tikulondezga ulongozgi wa Ciuta uwo uli mu Baibolo, tingaŵa ŵakukhorwa, ŵakukondwa, ndiposo ŵakuvikilirika.
w11-TB 5/1 31 ¶4
“Yehova Ndiye Muliska Wane”
Yehova wakuvikilira mberere zake. Para muliska palije, mberere zikucita wofi ndiposo zikusoŵa cakucita. Yehova wakuphalira ŵanthu ŵake kuti ŵaleke kopa nanga ni para ‘ŵakwenda mu cinkhwawo ca munkhorwe wa nyifwa,’ panji kuti panyengo yakuti ŵasuzgika comene. (Vesi 4) Yehova wakuŵalaŵilira ndipo ngwakunozgeka kuŵawovwira. Wangapa awo ŵakumusopa mahara na nkhongono izo ŵakukhumbikwira mwakuti ŵazizipizge viyezgo.—Ŵafilipi 4:13; Yakobe 1:2-5.
w11-TB 5/1 31 ¶5
“Yehova Ndiye Muliska Wane”
Yehova wakulyeska mberere zake. Mberere zikugomezga muliska kuti wazisangirenge cakurya. Tili na njara yauzimu, ndipo ni Yehova yekha uyo wangatilyeska. (Mateyu 5:3) Tikuwonga kuti Yehova wali na mtima wa kupa, ndipo wanozgera ŵateŵeti ŵake vyakurya vinandi. (Vesi 5) Baibolo ndiposo mabuku ghakulongosora Baibolo, nga ni magazini iyi mukuŵazga, ni vyakurya vyauzimu ivyo vikumazga njara yakuti timanye cifukwa ico Ciuta wali kutilengeras.
Vyo Twamanyila
w11-TB 2/15 24 ¶1-3
Temwani Urunji na Mtima Winu Wose
KWIZIRA mu Mazgu ghake na mzimu wake utuŵa, Yehova wakulongozga ŵanthu ŵake mu “nthowa za urunji.” (Sal. 23:3) Kweni pakuti tili ŵambura kufikapo, nyengo zinyake tikupatuka mu nthowa iyi. Tikwenera kufwilirapo kuti tambeso kucita ico nchakwenelera. Kasi nchivici cingatovwira? Nga ni Yesu, nase tikwenera kutemwa urunji.—Ŵazgani Salmo 45:6.
2 Kasi “nthowa za urunji” ni vici? “Nthowa” izo zikuyowoyeka apa ni malango ghaurunji gha Yehova agho munthu wakwenera kulondezga. Mu Cihebere na Cigiriki, lizgu lakuti “urunji” likuyowoya za cinthu ico “nchakunyoloka.” Lizgu ili likulongora kuti pakukhumbikwira kudemelera ku fundo izo ni ziwemi. Pakuti ‘urunji ni lufura lwa citengo ca Yehova,’ ŵateŵeti ŵake ŵakuthemba iyo kuti waŵalongozge mu nthowa ya kunyoloka.—Sal. 89:14.
3 Ciuta tingamukondweska pekha para tikuyezgayezga kulondezga fundo zake za urunji na mtima withu wose. (Dute. 32:4) Kuti ticite nthena tikwenera kusambira vyakukhwaskana na Yehova Ciuta kufuma mu Mazgu ghake, Baibolo. Para tikusambira vinandi vya Yehova na kusendelera kwa iyo zuŵa lililose, titemwenge comene urunji wake. (Yak. 4:8) Tikweneraso kulongozgeka na Mazgu gha Ciuta para tikusankha vinthu vyakuzirwa pa umoyo withu.
EPULELO 8-14
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 26–28
Vyo U Devedi Akabomba Ukuti Abukilile Ukuba Musubaliwa kwa Yehova
w04-CN 12/1 14 ¶8-9
Yendani mu Umphumphu
8 Davide anapemphera kuti: “Mundiyesere, Yehova, ndipo mundisunthe; yeretsani impso zanga ndi mtima wanga.” (Salmo 26:2) Impso zili m’katikati mwa thupi lathu. Impsozo, mophiphiritsira zimaimira maganizo a munthu a pansi penipeni pa mtima. Ndipo mtima wophiphiritsira umaimira m’kati mwa munthu, kapena kuti zimene zimamusonkhezera kuchita zinazake, mmene amamvera mumtima mwake, ndiponso nzeru zake. Popempha Yehova kuti amuyesere kapena kuti amuyese, Davide kwenikweni anali kupemphera kuti Yehova afufuze ndi kuyesa zoganiza zake za pansi pa mtima wake ndiponso mmene amamvera mumtima mwakemo.
9 Davide anapempha kuti impso ndi mtima wake ziyeretsedwe. Kodi Yehova amatiyeretsa motani m’kati mwathu? Davide anaimba kuti: “Ndidzadalitsa Yehova, amene anandichitira uphungu: Usikunso impso zanga zindilangiza.” (Salmo 16:7) Kodi izi zikutanthauzanji? Zikutanthauza kuti malangizo a Mulungu anam’fika pamtima Davide n’kukhazikika mumtimamo, ndi kukonza maganizo am’katikati mwa mtima wake. Zimenezi zingatichitikirenso ifeyo ngati timasinkhasinkha ndi mtima woyamikira malangizo amene timalandira kudzera m’Mawu a Mulungu, anthu omuimira, ndiponso gulu lake, ndi kulola kuti malangizowo akhazikike mumtima mwathu. Kupemphera nthawi zonse kwa Yehova kuti atiyeretse moteremu kungatithandize kuti tiyende mu umphumphu.
w04-CN 12/1 15 ¶12-13
Yendani mu Umphumphu
12 Pofotokoza chinthu chinanso chomwe chinalimbitsa umphumphu wake, Davide anati: “Sindinakhala pansi ndi anthu achabe; kapena kutsagana nawo anthu othyasika. Ndidana nawo msonkhano wa ochimwa, ndipo sindidzakhala nawo pansi ochita zoipa.” (Salmo 26:4, 5) Davide sankakhala pansi, ngakhale pang’ono chabe, ndi anthu oipa. Sankafuna kugwirizana nawo.
13 Nanga bwanji ifeyo? Kodi timakana kukhala ndi anthu achabe, kudzera m’mapulogalamu a pa TV, m’mavidiyo, m’makanema, pa Intaneti, kapena m’njira zina? Kodi timapewa anthu amene amabisa umunthu wawo? Anthu ena kusukulu kapena kuntchito kwathu anganamizire kuti ndi anzathu pamene ali ndi zolinga zachabe. Ndithudi, sitingafune kugwirizana ndi anthu amene sayenda m’choonadi cha Mulungu. Ngakhale kuti ampatuko amati ndi anthu oona mitima, nawonso angabise cholinga chawo pofuna kuti atisiyitse kutumikira Yehova. Kodi tingatani ngati mumpingo wachikristu muli ena amene ali ndi moyo wachiphamaso? Nawonso ndiye kuti amabisa umunthu wawo weniweni. Jayson, yemwe tsopano ndi mtumiki wotumikira, anali ndi anzake ngati amenewa ali wamng’ono. Pofotokoza za anthu amenewa, iye anati: “Tsiku lina mmodzi wa anzangawa anandiuza kuti: ‘Zimene timachita panopa zilibe ntchito chifukwa dziko latsopano likamadzafika, tidzakhala titafa basi. Sitidzadziwa kuti tikumanidwa chilichonse.’ Zimene ananenazi zinandigalamutsa. Ineyo sindikufuna kuti ndidzakhale nditafa dziko latsopano likamadzabwera.” Jayson anachita zanzeru posiya kugwirizana ndi anthu amenewa. Mtumwi Paulo anachenjeza motere: “Musanyengedwe; mayanjano oipa aipsa makhalidwe okoma.” (1 Akorinto 15:33) Motero kupewa kugwirizana ndi anthu oipa n’kofunika kwambiri.
w04-TB 12/1 16 ¶17-18
Yendani mu Umphumphu
17 Chihema, pamodzi ndi ntchito zake za nsembe, chinali likulu lolambirirapo Yehova ku Israyeli. Pofotokoza mmene ankasangalalira ndi malo amenewo, Davide anapemphera kuti: “Yehova, ndikonda chikhalidwe cha nyumba yanu, ndi malo akukhalamo ulemerero wanu.”—Salmo 26:8.
18 Kodi timakonda kusonkhana pamalo amene timaphunzira za Yehova? Nyumba ya Ufumu iliyonse, chifukwa cha maphunziro auzimu amene amachitikirapo, imakhala likulu la kulambira koona m’dera limene muli nyumbayo. Komanso, chaka n’chaka timakhala ndi misonkhano yachigawo, yadera, ndiponso masiku a misonkhano yapadera. Pamisonkhanoyi pamafotokozedwa “mboni,” kapena kuti zikumbutso za Yehova. Tikaphunzira ‘kuzikonda kwambiri’ zikumbutsozi, timakhala ofunitsitsa kupita kumisonkhano ndi kukatchera khutu tikafika kumisonkhanoko. (Salmo 119:167) N’zotsitsimutsa kwambiri kukhala ndi okhulupirira anzathu amene amadera nkhawa za moyo wathu ndiponso amene amatithandiza kupitiriza kuyenda mu umphumphu.—Ahebri 10:24, 25.
Vyo Twamanyila
w06-TB 7/15 28 ¶15
Yehova Amalanditsa Wovutika
15 Wamasalmo Davide anaimba kuti: “Pakuti wandisiya atate wanga ndi amayi wanga, koma Yehova anditola.” (Salmo 27:10) N’zolimbikitsa kudziwa kuti chikondi cha Yehova chimaposa cha kholo lina lililonse. Ngakhale kuti kukanidwa ndiponso kuzunzidwa ndi makolo kungakhale kowawa kwambiri, sikungasinthe mmene Yehova amatisamalirira. (Aroma 8:38, 39) Kumbukirani kuti Yehova amakoka munthu yemwe wakonda. (Yohane 3:16; 6:44) Zilibe kanthu kuti anthu akhala akukuchitirani zotani, Atate wanu wakumwamba amakukondani.
EPULELO 15-21
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 16–17
Ichilango Chikulangizya Ulughano lwa Yehova
it-1-E 802 ¶3
Kumaso
Ilizyu ilyakuti ‘ukufisa kumaso’ likung’anamulo ivintu ivyinji ukuyana na mo ivintu vibeleye. Nanti u Yehova u Chala afisa kumaso akinji vikung’anamula ukuti aleka ukuba nawe pabumanyani sona amaka ghache ghaleka ukubomba imbombo pa muntu uyo. Ichi chingaba chifukwa ichakusita ukwivwila kwa muntu weka pamo igulu ilya bantu, ngati mo vikabela nu luko ulwa Izilayeli. (Jobu 34.29; Sali. 30.5-8; Yesa. 54.8; 59.2) Akabalilo kamo u Yehova angifisa kumaso umwakuleka ukwivumbula mu mbombo pamo ukuleka ukwamula nu kulindilila akabalilo kache ko asalite. (Sali. 13.1-3) Po u Devedi akalaba ukuti, ‘Mufise kumaso kwinyu ichifukwa cha mbibi zyane’ apa akamulabagha u Chala ukuti amuhobokele imbibi zyache.—Sali. 51.9; yanisya nu Sali. 10.11.
w07-CN 3/1 19 ¶1
Osangalala Kudikira Yehova
Njira imene chilango cha Yehova chimatipindulitsira tingaiyerekezere ndi mmene zipatso zimakhwimira. Baibulo limanena mawu otsatirawa pankhani ya kulanga kwa Mulungu: “Kwa aja amene aphunzitsidwa nako, kumabala chipatso cha mtendere, ndicho chilungamo.” (Aheberi 12:11) Zipatso zimatenga nthawi kuti zipse, motero kusintha maganizo athu kuti agwirizane ndi zimene mawu a Mulungu amatiphunzitsa, kumatenganso nthawi. Mwachitsanzo, ngati khalidwe lathu linalake losayenera litachititsa kuti titaye mwayi winawake wotumikira mumpingo, mtima wodikira Mulungu ungatithandize kuti tisafooke kwambiri n’kufika potayiratu mtima. Pamenepa, mawu ouziridwa a Davide otsatirawa angatilimbikitse: “Mkwiyo [wa Mulungu] ukhala kanthawi kokha; koma kuyanja kwake moyo wonse. Kulira kuchezera, koma mamawa kuli kufuula kokondwera.” (Salmo 30:5) Tikakhala ndi mtima wodikira ndi kutsatira malangizo a Mawu a Mulungu ndi gulu lake, nthawi yathu ya “kufuula kokondwera” idzafika.
w21.10-TB 6 ¶18
Kasi Kung’anamuka Mtima Kwenecho Ni Vichi Chomenechomene?
18 Kuti walongore kuti ngwakupera nadi, munthu wakusezgeka nyengo zose wakwenera kwiza ku maungano na kulondezga ulongozgi uwo ŵalara ŵamupa wakuti walombenge na kusambira Baibolo payekha nyengo zose. Kweniso wagegenge kuchita vinthu ivyo vikamupangiska kuti wanange. Para waŵikapo mtima kuti wanozge ubwezi wake na Yehova, Yehova wamugowokerenge nadi ndipo ŵalara ŵamovwirenge kuti wawelereso mu mpingo. Kweni para ŵalara ŵakukhumba kumanya usange munthu ngwakupera nadi, ŵakwenera kumanya kuti nkhani zikuŵa zakupambana. Ntheura nkhani yiliyose ŵakwenera kuyiwona makora, ndipo ŵakwenera kugega kweruzga mwankhaza.
Vyo Twamanyila
w06-TB 6/1 31
Fundo Zikuru za Cigaŵa Cakwamba ca Buku la Masalmo
31:23—Kasi munthu wakujikuzga wakupokera wuli vyakuyanapo? Vyakuyanapo ivyo ŵakunena apa nchilango. Murunji wakupokera nchenyo kwa Yehova cifukwa ca kubuda mwangozi. Pakuti munthu wakujikuzga wakuleka yayi zakwananga zake, vyakuyanapo panji njombe yake nchilango cikuru.—Zintharika 11:31; 1 Petros 4:18.
EPULELO 22-28
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 32–33
Choni cho Chakulondiwa Ukulapa ku Mbibi?
w93-CN 3/15 9 ¶7
Chifundo cha Yehova Chimatipulumutsa Kukugwiritsidwa Mwala
7 Ngati tiri ndi liwongo la machimo aakulu a lamulo la Mulungu, tingakupeze kukhala kovuta kuulula machimo athu, ngakhale kwa Yehova. Kodi chingachitike nchiyani m’mikhalidwe yotero? Mu Salmo 32, Davide anavomereza kuti: ‘Pamene ndinakhala chete [mmalo mwakuulula] mafupa anga anakalamba ndi kubuula kwanga tsiku lonse. Chifukwa usana ndi usiku dzanja lanu [la Yehova] linandilemera ine; Uwisi wanga unasandulika kuuma kwa malimwe.’ (Vesi 3, 4) Kuyesa kubisa tchimo lake ndi kukanikiza chikumbumtima cha liwongo kunatopetsa Davide wochimwayo. Nkhaŵa inathetsa nyonga yake kwambiri kotero kuti anali wofanana ndi mtengo wa m’chilala wopanda madzi opatsa moyo. M’chenicheni, angakhale atakhala ndi ziyambukiro zovulaza mwa maganizo ndi mwakuthupi. Ndiiko komwe, iye anataya chisangalalo chake. Ngati aliyense wa ife agwera mumkhalidwe wofananawo, kodi tiyenera kuchitanji?
cl-TB 262 ¶8
Ciuta Uyo ‘Wakugowokera’
8 Davide wakayowoya mazgu agha wakati walapa: “Kwananga kwane nkhazomera panthazi pinu, ubendezi wane kuti nkhabisa cara; . . . ndipo penepapo mukagowokera uheni wa kwananga kwane.” (Salimo 32:5) Lizgu lakuti ‘kugowokera’ ndakufumira ku lizgu la Cihebere ilo likung’anamura “kuwuskapo” panji “kunyamura.” Pano lagwiliskirika nchito kung’anamura kuwuskapo “ubudi, majuvyo, na kwananga.” Mwantheura Yehova wakawuskapo zakwananga za Davide na kuzinyamulira kutali. Mwambura kukayika ici cikacepeska maghanoghano gha Davide gha kujiwona kuŵa wa wakawaka. (Salimo 32:3) Nase tingaŵa na cigomezgo cakukhora mwa Ciuta mweneuyo wakunyamulira kutali zakwananga za awo ŵakupenja cigowokero kwizira mu sembe ya Yesu ya kuwombora.—Mateyu 20:28.
w01-CN 6/1 30 ¶1
Kulapa Komwe Kumachiritsa
Davide atavomereza machimo ake sanadzione monga wopanda pake. Mawu ake m’masalmo omwe analemba onena za kuulula machimo, akusonyeza kuti anali womasuka ndi wotsimikiza kutumikira Mulungu mokhulupirika. Mwachitsanzo, taonani Salmo 32. Vesi 1 limati: “Wodala munthuyo wokhululukidwa tchimo lake; wokwiriridwa choipa chake.” Ngakhale tchimo litakhala lalikulu bwanji, zotsatira zake zimakhala zosangalatsa ngati munthu alapa moona mtima. Njira imodzi yosonyeza kuona mtima kumeneku, ndiyo kuvomereza zomwe tachita monga anachitira Davide. (2 Samueli 12:13) Iye sanapeze zifukwa zopeputsira kuchimwa kwake kwa Yehova kapena kuyesa kuloza ena chala. Vesi 5 likuti: “Ndinavomera choipa changa kwa Inu; ndipo mphulupulu yanga sindinaibisa. Ndinati, ndidzaululira Yehova machimo anga; ndipo munakhululukira choipa cha kulakwa kwanga.” Kulapa kwenikweni kumakhazikitsa mtima pansi, choncho munthu savutikanso ndi chikumbumtima chake poganiza zomwe anachita kale.
Vyo Twamanyila
w06-TB 6/1 31
Fundo Zikuru za Cigaŵa Cakwamba ca Buku la Masalmo
33:6; Kasi “mvuci” wa mulomo wa Yehova ni vici? Iyi ni nkhongono iyo Ciuta wakugwilira nchito, panji mzimu utuŵa, uwo wakagwiliskira nchito pakulenga macanya. (Genesis 1:1, 2) Mzimu ukucemeka mvuci wa mulomo wake cifukwa ungatumizgika kutali kukacita vinthu nga ni umo mvuci wankhongono ukufumira mu mulomo.
EPULELO 29–MEYI 5
AMAZYU GHA CHALA BUKABI | SALIMO 34–35
“Mumupalizyanje u Yehova Akabalilo Kosi”
w07-CN 3/1 22 ¶11
Tikweze Dzina la Yehova Pamodzi
11 “Ndidzalemekeza Yehova nyengo zonse; kum’lemekeza kwake kudzakhala m’kamwa mwanga kosalekeza.” (Salmo 34:1) Popeza Davide ankakhala mothawathawa, ayenera kuti ankada nkhawa kuti azipeza bwanji zosowa za moyo wake. Koma mawu amenewa akusonyeza kuti Davide anapitirizabe kukhala ndi mtima wofuna kulemekeza Yehova, ngakhale kuti anali ndi nkhawa zimenezi. Iye alidi chitsanzo chabwino kwa ife tikamakumana ndi mavuto. Kaya tili ku sukulu, ku ntchito, tili limodzi ndi Akhristu anzathu, kapena tikulalikira, cholinga chathu chachikulu chizikhala chofuna kulemekeza Yehova. Tangoganizirani zifukwa zambirimbiri zomwe tili nazo zochitira zimenezi. Mwachitsanzo, pali zinthu zambiri zomwe tingaziphunzire ndi kusangalala nazo m’chilengedwe cha Yehova chochititsa chidwichi. Ndipo taganizirani zimene Yehova wachita pogwiritsira ntchito mbali yapadziko lapansi ya gulu lake. Yehova wagwiritsira ntchito anthu okhulupirika kuchita zinthu zazikulu, ngakhale kuti ndi opanda ungwiro. Kodi ntchito za Mulungu tingaziyerekezere ndi za anthu amene dzikoli limawalambira? Kodi simukugwirizana ndi Davide, amene analemba kuti: “Pakati pa milungu palibe wina wonga Inu, Ambuye; ndipo palibe ntchito zonga zanu.”—Salmo 86:8.
w07-CN 3/1 22 ¶13
Tikweze Dzina la Yehova Pamodzi
13 “Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.” (Salmo 34:2) Apa, Davide sanali kudzitama chifukwa cha zinthu zimene anachita bwino. Mwachitsanzo, sanadzitame chifukwa cha mmene ananamizira mfumu ya ku Gati. Anazindikira kuti Yehova anam’teteza ali ku Gati, ndi kuti anathawa chifukwa cha thandizo lake. (Miyambo 21:1) Choncho Davide sanadzitame, koma anatamanda Yehova. Zimenezi zinachititsa anthu ofatsa kuyamba kukonda Yehova. Yesu nayenso anakweza dzina la Yehova, ndipo zimenezi zinachititsanso anthu odzichepetsa ndi ophunzitsika kuyamba kukonda Yehova. Masiku ano, anthu ofatsa a m’mayiko onse akulowa mu mpingo wapadziko lonse wa Akhristu odzozedwa, womwe Yesu ndiye Mutu wake. (Akolose 1:18) Anthu ofatsawa amakhudzidwa mtima akamva dzina la Mulungu likulemekezedwa ndi atumiki ake odzichepetsa ndiponso akamvetsetsa uthenga wa m’Baibulo mothandizidwa ndi mzimu woyera wa Mulungu.—Yohane 6:44; Machitidwe 16:14.
w07-CN 3/1 23 ¶15
Tikweze Dzina la Yehova Pamodzi
15 “Ndinafuna Yehova ndipo anandivomera, nandilanditsa m’mantha anga onse.” (Salmo 34:4) Zinthu ngati zimenezi zinali zofunika kwambiri kwa Davide. Choncho anawonjezera kuti: “Munthu uyu wozunzika anafuula, ndipo Yehova anamumva, nam’pulumutsa m’masautso ake onse.” (Salmo 34:6) Tikakhala ndi okhulupirira anzathu, timakhala ndi mipata yambiri yofotokoza zinthu zolimbikitsa zosonyeza momwe Yehova watithandizira kupirira mavuto. Zimenezi zimalimbitsa chikhulupiriro cha okhulupirira anzathu, monga momwe zimene Davide ananena zinalimbitsira chikhulupiriro cha anthu omwe anali ku mbali yake. Anthu omwe anali ndi Davide ‘anayang’ana [Yehova] nasanguluka: ndipo pankhope pawo sipanachite manyazi.’ (Salmo 34:5) Iwo sanachite manyazi ngakhale kuti ankathawa Mfumu Sauli. Anali ndi chikhulupiriro choti Mulungu anali ndi Davide, ndipo nkhope zawo zinali zosangalala. Mofanana ndi zimenezi, anthu amene akungophunzira kumene choonadi komanso amene akhala Akhristu kwa nthawi yaitali amadalira Yehova kuti awathandize. Popeza adzionera okha Yehova akuwathandiza, nkhope zawo n’zosangalala ndipo zimasonyeza kuti ndi otsimikiza mtima kukhalabe okhulupirika.
Vyo Twamanyila
w06-TB 6/1 31
Fundo Zikuru za Cigaŵa Cakwamba ca Buku la Masalmo
35:19—Kasi Davide wakang’anamurangaci apo wakapempha Ciuta kuti waleke kuzomerezga awo ŵakumutinkha kuti ŵaphayire jiso? Kuphayira jiso mphanyi cikalongora kuti ŵalwani ŵa Davide ŵakukondwa cifukwa cakuti ciŵembu ico ŵakamunozgera cafiskika. Davide wakapemphanga kuti ici cileke kucitika.