Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 9:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Patapita nthawi, Abimeleki+ mwana wa Yerubaala, anapita ku Sekemu kwa azichimwene awo a mayi ake. Ndipo anauza amalume akewo komanso banja lonse la bambo a mayi ake kuti: 2 “Chonde funsani atsogoleri* onse a ku Sekemu kuti, ‘Chabwino nʼchiyani kwa inu, kuti ana onse 70 a Yerubaala+ azikulamulirani, ndi kuti azikulamulirani munthu mmodzi? Ndipo musaiwale kuti ine ndi inu ndife magazi amodzi.’”*

  • 2 Samueli 11:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndi ndani anapha Abimeleki+ mwana wa Yerubeseti+ ku Tebezi? Kodi si mkazi amene anali pamwamba pa mpanda yemwe anaponya mwala wa mphero? Nʼchifukwa chiyani munauyandikira kwambiri mpandawo?’ Iwe ukanene kuti, ‘Nayenso mtumiki wanu Uriya Muhiti, wafa.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena