Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Levitiko 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zikondwerero za Yehova, kapena kuti misonkhano yopatulika imene muyenera kulengeza pa nthawi yake yoikidwiratu ndi iyi:

  • Numeri 28:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Numeri 29:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 “‘Pa tsiku loyamba la mwezi wa 7, muzichita msonkhano wopatulika. Musamagwire ntchito iliyonse yotopetsa.+ Tsiku limeneli lizikhala tsiku loliza lipenga.+

  • Deuteronomo 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Deuteronomo 16:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mwamuna aliyense pakati panu azikaonekera katatu pa chaka pamaso pa Yehova Mulungu wanu, pamalo amene Mulungu adzasankhe. Azikaonekera pa Chikondwerero cha Mkate Wopanda Zofufumitsa,+ Chikondwerero cha Masabata+ ndi pa Chikondwerero cha Misasa.+ Palibe aliyense wa iwo amene akuyenera kukaonekera kwa Yehova chimanjamanja.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani