Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Atasamuka kumeneko anakamanga msasa mʼdera la chigwa cha Arinoni, mʼchipululu chochokera kumalire a dziko la Aamori. Chigwa cha Arinoni+ chinali malire pakati pa dziko la Mowabu ndi la Aamori.

  • Oweruza 11:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako anatumiza uthenga kwa mfumu ya Edomu+ wakuti: “Tiloleni tidutse nawo mʼdziko lanu,” koma mfumu ya Edomu inakana. Anatumizanso uthenga kwa mfumu ya Mowabu,+ koma nayonso sinalole. Choncho Aisiraeli anapitiriza kukhala ku Kadesi.+ 18 Pamene ankadutsa mʼchipululu, analambalala dziko la Edomu+ ndi la Mowabu. Anadutsa chakumʼmawa kwa dziko la Mowabu+ nʼkukamanga misasa mʼchigawo cha Arinoni. Iwo sanadutse malire a Mowabu chifukwa Arinoni ndi amene anali malire a Mowabu.+

  • 2 Mbiri 20:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano Aamoni, Amowabu ndi anthu akudera lamapiri la Seiri+ abwera. Inu simunalole kuti Aisiraeli alowe mʼdziko lawo pamene ankachokera ku Iguputo ndipo sanawaphe.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani