Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 21:6-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno akulu onse amumzinda umene uli pafupi ndi munthu wakufayo azisamba mʼmanja+ pamwamba pa ngʼombe imene yathyoledwa khosi mʼchigwa ija. 7 Ndipo iwo azinena kuti, ‘Manja athu sanakhetse magazi awa, ndiponso maso athu sanaone magaziwa akukhetsedwa. 8 Inu Yehova, musaimbe mlanduwu anthu anu Aisiraeli amene munawawombola,+ ndipo musalole kuti mlandu wa magazi a munthu wosalakwa ukhale pa anthu anu Aisiraeli.’+ Akatero iwo sadzaimbidwa mlandu wa magaziwo. 9 Mukadzachita zimenezi mudzachotsa mlandu wa magazi a munthu wosalakwa pakati panu, chifukwa mudzakhala mutachita zinthu zoyenera pamaso pa Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani