Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yoswa 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mzindawu komanso zinthu zonse zimene zilimo ziyenera kuwonongedwa,+ zonse ndi za Yehova. Rahabi+ yekha, hule uja, musamuphe. Mumusiye pamodzi ndi onse amene ali nawo mʼnyumba mwake, chifukwa iye anabisa anthu amene tinawatuma.+

  • Yoswa 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsiku limenelo, Yoswa analanda mzinda wa Makeda+ ndipo anapha anthu amumzindawo ndi lupanga. Anapha mfumu ya mzindawo ndi anthu ake onse, ndipo anaonetsetsa kuti pasakhale wopulumuka.+ Mfumu ya ku Makeda+ anaichita zofanana ndi zomwe anaichita mfumu ya ku Yeriko.

  • Yoswa 11:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Aisiraeliwo anapha ndi lupanga munthu aliyense amene anali mumzindawo. Panalibe chamoyo chilichonse chimene chinatsala,+ ndipo Yoswa anatentha mzinda wa Hazori.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani