Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 13:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Sauli anasankha amuna 3,000 a mu Isiraeli. Pa amunawa, 2,000 anali ndi Sauliyo ku Mikimasi komanso kudera lamapiri la Beteli. Pamene amuna 1,000 anali ndi Yonatani+ ku Gibeya+ wa ku Benjamini. Anthu ena onse otsalawo anawauza kuti abwerere kumatenti awo. 3 Kenako Yonatani anapha asilikali a Afilisiti+ amene anali ku Geba+ ndipo Afilisiti anamva zimenezi. Zitatero Sauli analiza lipenga la nyanga ya nkhosa+ mʼdziko lonse nʼkunena kuti: “Tamverani Aheberi nonse!”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani