Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mbiri 11:12-14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Wotsatira wake anali Eliezara+ mwana wa Dodo, mwana wa Ahohi.+ Iye anali mmodzi wa asilikali atatu amphamvuwo. 13 Iye anali ndi Davide ku Pasi-damimu+ kumene Afilisiti anasonkhana kuti amenyane nawo. Kumeneko kunali munda wa balere wambiri ndipo anthu anali atathawa chifukwa choopa Afilisitiwo. 14 Koma iye anaima pakati pa mundawo nʼkuuteteza ndipo anapitiriza kupha Afilisiti, moti Yehova anawathandiza kuti apambane.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani