Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yoswa 20:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 1 Mafumu 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Solomo anali ndi nduna 12 zomwe zinkayangʼanira Aisiraeli onse ndipo zinkabweretsa chakudya kwa mfumu ndi banja lake. Nduna iliyonse inkabweretsa chakudya kwa mwezi umodzi pachaka.+

  • 1 Mafumu 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mwana wa Geberi ankayangʼanira ku Ramoti-giliyadi+ (dera lake linali midzi ingʼonoingʼono ya Yairi+ mwana wa Manase, yomwe ili ku Giliyadi.+ Analinso ndi chigawo cha Arigobi,+ chomwe chili ku Basana.+ Kunali mizinda ikuluikulu 60 yokhala ndi mipanda komanso zotchingira zakopa*).

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani