Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 18:23-27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Zedekiya+ mwana wa Kenaana anapita pomwe panali Mikaya+ nʼkumumenya mbama+ ndipo ananena kuti: “Zingatheke bwanji kuti mzimu wa Yehova undidutse nʼkukalankhula ndi iwe?”+ 24 Mikaya anayankha kuti: “Udzadziwa zimenezo tsiku limene udzalowe mʼchipinda chamkati kukabisala.” 25 Ndiyeno mfumu ya Isiraeli inati: “Mtengeni Mikaya mupite naye kwa Amoni mkulu wa mzinda ndi Yowasi mwana wa mfumu. 26 Mukawauze kuti, ‘Mfumu yanena kuti: “Mʼtsekereni munthu uyu.+ Muzimʼpatsa chakudya chochepa ndi madzi ochepa mpaka nditabwerako mwamtendere.”’” 27 Koma Mikaya anati: “Mukakabwerakodi mwamtendere ndiye kuti Yehova sanalankhule nane.”+ Ananenanso kuti: “Anthu inu, mawu angawa muwakumbukire.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani