Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Samueli 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Davide anakhazikitsa midzi ya asilikali ku Edomu. Mu Edomu monse anaikamo midzi ya asilikali, moti Aedomu anakhala antchito a Davide+ ndipo Yehova ankathandiza Davide kuti apambane kulikonse kumene wapita.+

  • 2 Mafumu 8:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mʼmasiku a Yehoramu, Aedomu anagalukira Yuda+ ndipo kenako anasankha mfumu yoti iziwalamulira.+ 21 Choncho Yehoramu anapita ku Zairi pamodzi ndi magaleta ake onse. Kumeneko, iye ananyamuka usiku nʼkukapha Aedomu amene anamuzungulira. Anaphanso atsogoleri a asilikali okwera magaleta ndipo asilikali ena onse anathawira kumatenti awo. 22 Koma Aedomu anapitirizabe kugalukira Yuda mpaka lero. Pa nthawi imeneyi mʼpamenenso Libina+ anagalukira Yuda.

  • Salimo 108:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani