Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mfumu Solomo inapanganso zombo ku Ezioni-geberi+ pafupi ndi Eloti, pagombe la Nyanja Yofiira, mʼdziko la Edomu.+

  • 2 Mbiri 20:35-37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kenako Yehosafati mfumu ya Yuda anachita mgwirizano ndi Ahaziya mfumu ya Isiraeli amene ankachita zoipa.+ 36 Choncho anayamba kugwira naye ntchito yopanga zombo zopita ku Tarisi.+ Zombozo anazipangira ku Ezioni-geberi.+ 37 Koma Eliezere mwana wa Dodavahu wa ku Maresa analosera zinthu zotsutsana ndi Yehosafati kuti: “Chifukwa chakuti mwachita mgwirizano ndi Ahaziya, Yehova awononga ntchito yanu.”+ Choncho zombozo zinasweka+ ndipo sizinathenso kupita ku Tarisi.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani