-
Yoswa 19:46Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
46 Me-jarikoni ndi Rakoni, nʼkukafika kumalire amene ali kutsogolo kwa Yopa.+
-
-
Yoswa 19:48Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
48 Ichi chinali cholowa cha fuko la Dani motsatira mabanja awo, ndipo imeneyi inali mizinda yawo ndi midzi yake.
-
-
Ezara 3:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Kenako anthuwo anapereka ndalama kwa anthu osema miyala+ ndi amisiri.+ Anaperekanso chakudya, zakumwa ndi mafuta kwa anthu a ku Sidoni ndi ku Turo chifukwa anabweretsa matabwa a mkungudza kudzera panyanja kuchokera ku Lebanoni kukafika ku Yopa.+ Anachita zimenezi mogwirizana ndi chilolezo chimene Koresi mfumu ya ku Perisiya anawapatsa.+
-