Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nehemiya 6:10-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako ndinapita kunyumba kwa Semaya mwana wa Delaya, mwana wa Mehetabele, amene anali atadzitsekera mʼnyumba. Iye anandiuza kuti: “Tiye tigwirizane nthawi yoti tikakumane kunyumba ya Mulungu woona, mʼkachisi ndipo tikatseke zitseko za kachisiyo. Chifukwa akubwera kudzakupha, akubwera kudzakupha usiku.” 11 Koma ndinamuyankha kuti: “Kodi mwamuna ngati ine ndingathawe? Kodi munthu ngati ine angalowe mʼkachisi nʼkukhala ndi moyo?+ Ine sindikalowamo!” 12 Kenako ndinazindikira kuti sanatumidwe ndi Mulungu, koma Tobia ndi Sanibalati+ ndi amene anamulemba ganyu kuti andinamize ndi ulosi wabodzawu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani