Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 8:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zimenezi ndi zimene zidzachitikire* anthu onse amene aiwala Mulungu,

      Chifukwa chiyembekezo cha anthu oipa* chidzatha.

      14 Amene amadalira zinthu zosathandiza,

      Amene amadalira zinthu zosalimba ngati ulusi wa kangaude.*

  • Yobu 11:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma maso a anthu oipa sadzaonanso,

      Ndipo sadzapeza malo othawirako,

      Chiyembekezo chawo chidzakhala imfa* basi.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani