Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Miyambo 22:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Usabere munthu wosauka chifukwa choti ndi wosauka,+

      Ndipo usapondereze munthu wonyozeka pageti la mzinda,+

  • Amosi 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chifukwa ndikudziwa kuchuluka kwa zochita zanu zondigalukira,

      Ndiponso kukula kwa machimo anu.

      Mumachitira nkhanza munthu wolungama,

      Mumalandira ziphuphu,

      Komanso mumaphwanya ufulu wa anthu osauka pageti la mzinda.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani