-
Yeremiya 46:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Inu mahatchi pitani.
Inu magaleta thamangani ndi liwiro lalikulu!
-
-
Yeremiya 47:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Abambo adzathawa osayangʼana mʼmbuyo kuti apulumutse ana awo.
Adzachita zimenezi chifukwa manja awo adzafooka,
Akadzamva mgugu wa mahatchi a adani awo,
Akadzamva phokoso la magaleta ankhondo a adani awo
Komanso kulira kwa mawilo ake,
-
Habakuku 1:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Mahatchi ake ankhondo amathamanga kwambiri.
Mahatchi awo amachokera kutali.
Ndipo amauluka ngati chiwombankhanga chimene chikuthamanga kuti chikapeze chakudya.+
-
-
-