Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Miyambo 21:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 46:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu mahatchi pitani.

      Inu magaleta thamangani ndi liwiro lalikulu!

      Lolani asilikali kuti apite.

      Lolani Kusi ndi Puti amene amadziwa kugwiritsa ntchito chishango kuti apite,+

      Komanso anthu a ku Ludimu+ amene amadziwa kukunga ndi kuponya uta.+

  • Yeremiya 47:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Abambo adzathawa osayangʼana mʼmbuyo kuti apulumutse ana awo.

      Adzachita zimenezi chifukwa manja awo adzafooka,

      Akadzamva mgugu wa mahatchi a adani awo,

      Akadzamva phokoso la magaleta ankhondo a adani awo

      Komanso kulira kwa mawilo ake,

  • Habakuku 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mahatchi* ake ndi aliwiro kuposa akambuku,

      Ndi oopsa kuposa mimbulu usiku.+

      Mahatchi ake ankhondo amathamanga kwambiri.

      Mahatchi awo amachokera kutali.

      Ndipo amauluka ngati chiwombankhanga chimene chikuthamanga kuti chikapeze chakudya.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani