Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Samueli 19:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Nthawi yomweyo, Mikala anathandiza Davide kuti atulukire pawindo nʼkuthawa.

  • Salimo 18:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Iye amandipulumutsa kwa adani anga olusa.

      Mumandikweza pamwamba pa anthu amene amandiukira.+

      Mumandipulumutsa kwa munthu wachiwawa.

  • Salimo 71:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inu Mulungu wanga, ndipulumutseni mʼmanja mwa woipa,+

      Kuti ndisagwidwe ndi munthu wochita zinthu mopondereza komanso wopanda chilungamo.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani