Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 25:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Inu Mulungu wanga, ndimakudalirani.+

      Musalole kuti ndichite manyazi.+

      Musalole kuti adani anga asangalale chifukwa cha mavuto anga.+

  • Salimo 31:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 45:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma Isiraeli adzapulumutsidwa ndi Yehova ndipo chipulumutso chake chidzakhala chosatha.+

      Inu simudzachititsidwa manyazi kapena kunyozeka mpaka kalekale.+

  • Yeremiya 17:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Anthu amene amandizunza achite manyazi,+

      Koma musalole kuti ineyo ndichite manyazi.

      Anthuwo agwidwe ndi mantha aakulu,

      Koma musalole kuti ine ndigwidwe ndi mantha aakulu.

      Agwetsereni tsoka,+

      Ndipo muwaphwanye komanso kuwawononga mpaka atheretu.*

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani