Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Eliya*+ wa ku Tisibe, wochokera ku Giliyadi anauza Ahabu+ kuti: “Ndikulumbira mʼdzina la Yehova Mulungu wamoyo, Mulungu wa Isiraeli amene ndimamʼtumikira, sikubwera mame kapena mvula zaka zikubwerazi, pokhapokha ine nditanena.”+

  • 1 Mafumu 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma patapita masiku angapo,+ mtsinjewo unauma chifukwa mʼdzikomo simunkagwa mvula.

  • Yesaya 42:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndidzawononga mapiri ndi zitunda

      Ndi kuumitsa zomera zonse zimene zili mmenemo.

      Mitsinje ndidzaisandutsa zilumba*

      Ndipo ndidzaumitsa madambo onse amadzi.+

  • Amosi 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani