Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 7:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iye adzakukondani, kukudalitsani komanso kukuchulukitsani. Adzakudalitsani ndithu pokupatsani ana ambiri,*+ adzadalitsa zokolola za nthaka yanu, mbewu zanu, vinyo wanu watsopano, mafuta anu,+ ana a ngʼombe zanu ndi ana a nkhosa zanu, mʼdziko limene analumbira kwa makolo anu kuti adzakupatsani.+ 14 Inu mudzakhala odalitsika kwambiri mwa anthu onse.+ Pakati panu sipadzapezeka mwamuna, mkazi kapena chiweto chosabereka.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani