Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mbiri 10:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 53:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Koma adzagwidwa ndi mantha aakulu,

      Mantha amene sanayambe agwidwapo chiyambire,*

      Chifukwa Mulungu adzamwaza mafupa a anthu amene akukuukirani.*

      Mudzawachititsa manyazi chifukwa Yehova wawakana.

  • Yesaya 59:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Njira ya mtendere sakuidziwa,

      Ndipo mʼnjira zawo mulibe chilungamo.+

      Misewu yawo aikhotetsakhotetsa.

      Palibe munthu aliyense woyenda mmenemo amene adzadziwe mtendere.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani