Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 51:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Iwe mkazi amene ukukhala pamadzi ambiri,+

      Amene uli ndi chuma chambiri,+

      Mapeto ako afika ndipo nthawi yako yopanga phindu yatha.+

  • Ezekieli 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho ndinapita kwa anthu amene anatengedwa kupita ku ukapolo omwe anali ku Tele-abibu. Anthuwa ankakhala pafupi ndi mtsinje wa Kebara.+ Ndinakhala nawo kumeneko masiku 7 nditasokonezeka maganizo.+

  • Danieli 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa tsiku la 24 la mwezi woyamba, ndili mʼmbali mwa mtsinje waukulu, mtsinje wa Tigirisi,*+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani