Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Samueli 6:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Davide ndi anthu onse a nyumba ya Isiraeli ankasangalala pamaso pa Yehova, akuimba mitundu yonse ya zoimbira za mtengo wofanana ndi mtengo wa mkungudza. Ankaimbanso zeze, zoimbira za zingwe,+ zinganga+ ndi maseche+ osiyanasiyana.

  • 1 Mbiri 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Hemani,+ Asafu+ ndi Etani anawasankha kuti aziimba ndi zinganga zakopa.*+

  • 1 Mbiri 16:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mtsogoleri wawo anali Asafu,+ wachiwiri wake anali Zekariya. Ndipo Yeyeli, Semiramoti, Yehiela, Matitiya, Eliyabu, Benaya, Obedi-edomu ndi Yeyeli+ ankaimba ndi zoimbira za zingwe ndiponso azeze.+ Asafu ankaimba zinganga.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani