Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Samueli 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Samueli 12:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Miyambo 6:32-35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Aliyense wochita chigololo ndi mkazi ndi wopanda nzeru.*

      Amene amachita zimenezi amadzibweretsera mavuto aakulu pa moyo wake.+

      33 Adzangodzivulaza yekha ndipo anthu adzamunyoza,+

      Moti kunyozeka kwake sikudzafufutika.+

      34 Chifukwa nsanje imachititsa kuti mwamuna wake akwiye kwambiri.

      Pomubwezera sadzamva chisoni.+

      35 Iye sadzavomera chipukuta misozi chilichonse,*

      Ndipo sadzapepeseka ngakhale utapereka mphatso yaikulu bwanji.

  • Aheberi 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani