Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Esitere 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho Hamani anamupachika pamtengo umene anakonzera Moredikayi, ndipo mkwiyo wa mfumu unatha.

  • Salimo 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mitundu ya anthu yagwera mʼdzenje limene anakumba okha.

      Phazi lawo lakodwa mu ukonde umene anatchera okha.+

  • Miyambo 28:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Munthu amene amasocheretsa anthu owongoka mtima kuti azichita zinthu zoipa, adzagwera mʼdzenje lake lomwe,+

      Koma anthu osalakwa adzalandira zinthu zabwino.+

  • Mlaliki 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Amene akukumba dzenje angathe kugweramo+ ndipo amene akugumula mpanda wamiyala angathe kulumidwa ndi njoka.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani