Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nehemiya 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Masiku amenewo ndinaona anthu ku Yuda akuponda moponderamo mphesa pa tsiku la Sabata.+ Ankabweretsa mbewu ndipo ankazikweza pa abulu. Ankabweretsanso vinyo, mphesa, nkhuyu ndi katundu wosiyanasiyana ku Yerusalemu pa tsiku la Sabata.+ Choncho ndinawadzudzula pa nkhani yogulitsa zinthu pa tsiku limenelo.*

  • Yesaya 56:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Wosangalala ndi munthu amene amachita zimenezi,

      Ndiponso mwana wa munthu amene amatsatira zimenezi,

      Amene amasunga Sabata ndipo salidetsa+

      Komanso amaletsa dzanja lake kuti lisachite choipa chilichonse.

  • Yeremiya 17:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova wanena kuti: “Samalani kuti musanyamule katundu aliyense kapena kulowa naye pamageti a Yerusalemu pa tsiku la Sabata.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani