-
Nehemiya 13:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Masiku amenewo ndinaona anthu ku Yuda akuponda moponderamo mphesa pa tsiku la Sabata.+ Ankabweretsa mbewu ndipo ankazikweza pa abulu. Ankabweretsanso vinyo, mphesa, nkhuyu ndi katundu wosiyanasiyana ku Yerusalemu pa tsiku la Sabata.+ Choncho ndinawadzudzula pa nkhani yogulitsa zinthu pa tsiku limenelo.*
-
-
Yesaya 56:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Wosangalala ndi munthu amene amachita zimenezi,
Ndiponso mwana wa munthu amene amatsatira zimenezi,
Amene amasunga Sabata ndipo salidetsa+
Komanso amaletsa dzanja lake kuti lisachite choipa chilichonse.
-
-
Yeremiya 17:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Yehova wanena kuti: “Samalani kuti musanyamule katundu aliyense kapena kulowa naye pamageti a Yerusalemu pa tsiku la Sabata.+
-