-
Yesaya 7:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Mwanayo asanafike podziwa kukana choipa ndi kusankha chabwino, mayiko a mafumu awiri amene ukuchita nawo manthawo, adzakhala atasiyidwiratu.+
-
-
Yesaya 8:3, 4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Kenako ndinagona ndi mneneri wamkazi* ndipo anakhala woyembekezera. Pambuyo pake anabereka mwana wamwamuna.+ Ndiyeno Yehova anandiuza kuti: “Umupatse dzina lakuti Maheri-salala-hasi-bazi, 4 chifukwa mwanayo asanadziwe kuitana kuti, ‘Ababa!’ kapena ‘Amama!’ chuma cha ku Damasiko ndi katundu wolandidwa ku Samariya zidzatengedwa nʼkupita nazo kwa mfumu ya Asuri.”+
-