Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Kwezani chizindikiro choloza njira ya ku Ziyoni.

      Thawirani kumalo otetezeka, musangoima,”

      Chifukwa ndikubweretsa tsoka kuchokera kumpoto,+ tsoka lalikulu kwambiri.

  • Ezekieli 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mʼmalo onse amene mukukhala, mizinda idzawonongedwa.+ Malo okwezeka adzagumulidwa ndipo adzakhala mabwinja.+ Maguwa anu ansembe adzagumulidwa nʼkuphwanyidwa. Mafano anu onyansa adzawonongedwa, maguwa anu ofukizirapo zonunkhira adzagwetsedwa ndipo ntchito za manja anu zidzawonongedwa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani