Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 9:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndikanakonda ndikanakhala ndi malo ogona anthu apaulendo mʼchipululu.

      Zikanatero, ndikanasiya anthu a mtundu wanga nʼkuwachokera,

      Chifukwa onse ndi achigololo,+

      Gulu la anthu ochita zachinyengo.

       3 Iwo ndi okonzeka kunama ngati uta umene wakungidwa.

      Dzikolo ladzaza ndi chinyengo ndipo palibe amene ali wokhulupirika.+

      “Iwo akuchita zoipa motsatizanatsatizana,

      Ndipo akundinyalanyaza,”+ akutero Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani