Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 40:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mmisiri amapanga fano lachitsulo,*

      Mmisiri wina wa zitsulo amachikuta ndi golide,+

      Ndipo amachipangira matcheni asiliva.

  • Yesaya 41:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Choncho mmisiri wa mitengo akulimbikitsa mmisiri wa zitsulo.+

      Amene amawongola zitsulo ndi hamala

      Akulimbikitsa munthu amene akusula zitsulo ndi hamala.

      Ponena za ntchito yowotcherera zitsulo ndi mtovu, iye akuti: “Zili bwino.”

      Kenako amakhomerera fanolo ndi misomali kuti lisagwe.

  • Yeremiya 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Miyambo ya anthu amenewa ndi yopanda pake.

      Mmisiri amagwetsa mtengo munkhalango,

      Nʼkusema fano pogwiritsa ntchito chida chake.*+

  • Hoseya 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Machitidwe 17:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani