Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 48:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mowabu sakutamandidwanso.

      Ku Hesiboni+ adani amukonzera chiwembu kuti amuwononge ndipo akunena kuti:

      ‘Bwerani, tiyeni timuwononge kuti asakhalenso mtundu wa anthu.’

      Iwenso Madimeni khala chete,

      Chifukwa lupanga likukutsatira.

       3 Ku Horonaimu+ kwamveka kulira kofuula,

      Kwamveka phokoso lachiwonongeko ndi kugwa kwakukulu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani