Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Iwo akubwera kuchokera kudziko lakutali,+

      Kuchokera kumalo akutali kwambiri pansi pa thambo,

      Yehova akubwera ndi zida zamkwiyo wake,

      Kuti awononge dziko lonse lapansi.+

  • Yeremiya 51:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Nolani mivi yanu.*+ Tengani zishango zozungulira.

      Yehova walimbikitsa* mafumu a Amedi kuti akamenye nkhondo,+

      Chifukwa akufuna kuwononga Babulo.

      Yehova akubwezera Babulo, akumubwezera chifukwa cha kachisi wake.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani