Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 45:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndidzakupatsa chuma chimene chili mumdima

      Ndiponso chuma chimene chabisidwa mʼmalo achinsinsi,+

      Kuti udziwe kuti ine ndine Yehova,

      Mulungu wa Isiraeli, amene ndikukuitana pokutchula dzina lako.+

  • Yeremiya 50:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Lupanga lidzawononga mahatchi awo, magaleta awo ankhondo

      Ndi anthu onse a mitundu yosiyanasiyana amene ali pakati pawo

      Ndipo adzakhala ngati akazi.+

      Lupanga lidzawononga chuma chake ndipo anthu ena adzachitenga.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani