Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 136:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Miyambo 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 40:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 10:12-16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iye ndi Mulungu amene anapanga dziko lapansi pogwiritsa ntchito mphamvu zake,

      Amene anakhazikitsa dziko lapansi pogwiritsa ntchito nzeru zake.+

      Amenenso anatambasula kumwamba chifukwa cha kuzindikira kwake.+

      13 Mawu ake akamveka,

      Madzi akumwamba amachita mkokomo,+

      Ndipo amachititsa mitambo* kukwera kuchokera kumalekezero a dziko lapansi.+

      Iye amachititsa kuti kukamagwa mvula mphezi zizingʼanima,

      Ndipo amatulutsa mphepo mʼnyumba zake zosungira.+

      14 Munthu aliyense akuchita zinthu mopanda nzeru komanso mosazindikira.

      Mmisiri wa zitsulo aliyense adzachita manyazi chifukwa cha chifaniziro chake chosula.+

      Chifukwa chifaniziro chake chopangidwa ndi chitsulo chosungunula ndi mulungu wonama

      Ndipo mafano amenewa alibe mzimu.*+

      15 Iwo ndi achabechabe, oyenera kunyozedwa.+

      Tsiku loti aweruzidwe likadzafika adzawonongedwa.

      16 Koma Mulungu, amene ndi cholowa cha Yakobo, sali ngati mafano amenewa,

      Chifukwa iye ndi amene anapanga china chilichonse,

      Ndipo Isiraeli ndi ndodo ya cholowa chake.+

      Dzina lake ndi Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani