Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 50:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova, mʼdzikomo simudzakhalanso anthu.+

      Dziko lonselo lidzakhala bwinja.+

      Aliyense wodutsa pafupi ndi Babulo adzayangʼanitsitsa mwamantha

      Ndipo adzamuimbira mluzu chifukwa cha miliri yake yonse.+

  • Yeremiya 50:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 “Mofanana ndi mmene Mulungu anawonongera Sodomu ndi Gomora+ komanso midzi imene anali nayo pafupi,+ ndi mmenenso zidzakhalire ndi Babulo. Palibe aliyense amene adzakhalenso mumzindawo,”+ akutero Yehova.

  • Chivumbulutso 18:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani