Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 13:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Uwu ndi uthenga wokhudza Babulo,+ umene Yesaya+ mwana wa Amozi anaona mʼmasomphenya:

  • Yesaya 13:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 MʼBabulo simudzakhalanso anthu,

      Ndipo sadzakhalanso malo oti anthu nʼkukhalamo ku mibadwo yonse.+

      Kumeneko Mluya sadzakhomako tenti yake

      Ndipo abusa sadzagonekako ziweto zawo.

  • Yeremiya 50:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Choncho nyama zamʼchipululu zidzakhala mmenemo pamodzi ndi nyama zolira mokuwa,

      Ndipo nthiwatiwa zidzakhala mmenemo.+

      Mumzindawo simudzakhalanso munthu aliyense,

      Ndipo sudzakhala malo oti munthu nʼkukhalamo ku mibadwo yonse.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani