Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chisoni changa nʼchosachiritsika.

      Mtima wanga ukudwala.

  • Yeremiya 8:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndasweka mtima chifukwa cha kuwonongeka kwa mwana wamkazi wa anthu anga.+

      Ndine wachisoni.

      Ndipo ndili ndi mantha aakulu.

  • Yeremiya 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndikanakonda mʼmutu mwanga mukanakhala madzi ambiri,

      Ndiponso maso anga akanakhala kasupe wa misozi.+

      Zikanatero, ndikanalira masana ndi usiku

      Chifukwa cha anthu a mtundu wanga amene aphedwa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani