Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mafumu 25:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 52:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mʼmwezi wa 5, pa tsiku la 10 la mweziwo, chomwe chinali chaka cha 19 cha Mfumu Nebukadinezara* ya ku Babulo, Nebuzaradani mkulu wa asilikali olondera mfumu, amene anali mtumiki wa mfumu ya Babulo, anabwera ku Yerusalemu.+

  • Yeremiya 52:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Nebuzaradani mkulu wa asilikali olondera mfumu anatenga ena mwa anthu onyozeka ndiponso anthu ena onse amene anatsala mumzindawo. Anatenganso anthu amene anathawira kwa mfumu ya Babulo komanso amisiri onse aluso nʼkupita nawo ku ukapolo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani