Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Oweruza 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Udzakhala ndi pakati ndipo udzabereka mwana wamwamuna. Mʼmutu mwake musadzadutse lezala+ chifukwa mwanayo adzakhala Mnaziri* wa Mulungu kuchokera tsiku limene adzabadwe.* Iye adzatsogolera populumutsa Isiraeli mʼmanja mwa Afilisiti.”+

  • Salimo 139:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mafupa anga sanali obisika kwa inu

      Pa nthawi imene ndinkapangidwa kumalo amene aliyense sakanatha kuona,

      Pamene munkandiwomba ngati nsalu mʼmalo apansi kwambiri padziko lapansi.+

      16 Maso anu anandiona ngakhale pamene ndinali mluza.*

      Ziwalo zanga zonse zinalembedwa mʼbuku lanu

      Mʼbukumo munalembedwa za masiku amene zinapangidwa,

      Zinalembedwa chiwalo chilichonse chisanapangidwe.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani