-
Yeremiya 22:28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Kodi munthu uyu Koniya, wangokhala chiwiya chonyozeka komanso chophwanyika,
Chiwiya chimene palibe amene akuchifuna?
Nʼchifukwa chiyani iyeyu ndi ana ake agwetsedwa pansi
Nʼkuponyedwa mʼdziko limene sakulidziwa?’+
-