Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Levitiko 26:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 5:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iye waikira chizindikiro mtundu wakutali.+

      Wauimbira likhweru kuti ubwere kuchokera kumapeto kwa dziko lapansi.+

      Ndipotu mtunduwo ukubwera mofulumira kwambiri.+

  • Yeremiya 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova wanena kuti, ‘Ndikuitana mafuko onse a maufumu a kumpoto.+

      Iwo adzabwera ndipo aliyense adzakhazikitsa mpando wake wachifumu,

      Pakhomo la mageti a Yerusalemu.+

      Iwo adzaukira mpanda wake wonse

      Ndi mizinda yonse ya Yuda.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani