Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 21:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Manase anaphanso anthu ambiri osalakwa mpaka magazi awo anadzaza Yerusalemu kuyambira koyambirira mpaka kumapeto,+ kuwonjezera pa tchimo lake lochititsa kuti Ayuda achimwe pochita zoipa pamaso pa Yehova.

  • Salimo 106:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Ankakhetsa magazi a anthu osalakwa,+

      Magazi a ana awo aamuna komanso a ana awo aakazi,

      Amene anawapereka nsembe kwa mafano a ku Kanani.+

      Ndipo dzikolo linaipa ndi magazi amene iwo anakhetsa.

  • Yesaya 10:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsoka kwa amene akukhazikitsa malamulo oipa,+

      Amene amangokhalira kulemba malamulo opondereza,

       2 Kuti asamvetsere mlandu wa anthu osauka

      Ndiponso kuti asachitire chilungamo anthu onyozeka amene ali pakati pa anthu anga.+

      Amalanda katundu wa akazi amasiye

      Komanso katundu wa ana amasiye.+

  • Mateyu 23:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani