Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 27:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Yehova wandiuza kuti, ‘Upange zomangira komanso magoli ndipo uzivale mʼkhosi mwako. 3 Kenako uzitumize kwa mfumu ya Edomu,+ mfumu ya Mowabu,+ mfumu ya Aamoni,+ mfumu ya Turo+ ndi mfumu ya Sidoni.+ Upatsire amithenga amene abwera ku Yerusalemu kudzaonana ndi Zedekiya mfumu ya Yuda.

  • Yeremiya 47:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Chifukwa tsiku limene likubweralo lidzawononga Afilisiti+ onse.

      Lidzawononga aliyense wotsala amene akuthandiza Turo+ ndi Sidoni.+

      Chifukwa Yehova adzawononga Afilisiti,

      Amene ndi otsala ochokera pachilumba cha Kafitori.*+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani