Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 36:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova Mulungu wa makolo awo anapitiriza kuwachenjeza kudzera mwa atumiki ake. Ankawachenjeza mobwerezabwereza chifukwa ankamvera chisoni anthu akewo ndiponso malo ake okhala. 16 Koma iwo anapitiriza kunyoza atumiki a Mulungu woona,+ kunyoza mawu ake+ ndiponso kuseka aneneri ake.+ Iwo anafika poti panalibenso chiyembekezo choti angathe kuchiritsidwa. Kenako Yehova anawakwiyira kwambiri nʼkuwalanga.+

  • Yesaya 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 8:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndasweka mtima chifukwa cha kuwonongeka kwa mwana wamkazi wa anthu anga.+

      Ndine wachisoni.

      Ndipo ndili ndi mantha aakulu.

      22 Kodi mu Giliyadi mulibe mafuta a basamu?+

      Kapena kodi mulibe wochiritsa* mmenemo?+

      Nʼchifukwa chiyani mwana wamkazi wa anthu anga sanachiritsidwe?+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani