Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 4:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Popeza tsopano wawonongedwa, ndiye utani?

      Unkakonda kuvala zovala zamtengo wapatali,*

      Kudzikongoletsa ndi zokongoletsera zagolide

      Ndiponso kukongoletsa mʼmaso mwako ndi penti wakuda.

      Koma unkangotaya nthawi yako pachabe podzikongoletsa.+

      Amene ankakufuna akukana

      Ndipo tsopano akufuna kukupha.+

  • Ezekieli 16:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 ine ndikusonkhanitsa pamodzi zibwenzi zako zonse zimene unkazisangalatsa, onse amene unkawakonda limodzi ndi onse amene unkadana nawo. Ndidzawasonkhanitsa pamodzi kuchokera kumadera onse ozungulira kuti akuukire ndipo ndidzakuvula kuti aone maliseche ako, moti adzakuona uli mbulanda.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani