Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ezekieli 45:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 “‘Mukamagawana dzikoli kuti likhale cholowa chanu,+ mudzatenge malo ena nʼkuwapereka kwa Yehova monga gawo loyera.+ Malowo adzakhale mikono 25,000* mulitali ndi mikono 10,000 mulifupi.+ Malo onsewo* adzakhale gawo loyera. 2 Mkati mwa gawo loyeralo mudzakhale malo ofanana mbali zonse kuti adzakhale malo oyera. Malowa adzakhale mikono 500 mbali zonse*+ ndipo kumbali iliyonse kudzakhale malo odyetserako ziweto okwana mikono 50.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani