Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 59:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ukonde wawo wa kangaude sudzakhala chovala chawo,

      Ndipo zochita zawo sizingawathandize.+

      Ntchito zawo nʼzopweteka ena,

      Ndipo mʼmanja mwawo muli ntchito zachiwawa.+

  • Mika 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwo amalakalaka minda ya anthu ena ndipo amaitenga.+

      Amalakalakanso nyumba za anthu ena nʼkuzitenga.

      Amatenga mwachinyengo nyumba ya munthu,+

      Ndipo amatenganso cholowa cha munthu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani