Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ezekieli 7:15-17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Lupanga lidzapha anthu amene ali kunja kwa mzinda+ ndipo mliri ndi njala zidzapha amene ali mkati mwa mzinda. Aliyense amene ali kunja kwa mzinda adzaphedwa ndi lupanga ndipo amene ali mumzinda adzafa ndi njala komanso mliri.+ 16 Anthu awo amene adzapulumuke adzathawira kumapiri ndipo mofanana ndi njiwa zamʼzigwa, aliyense adzalira chifukwa cha zolakwa zake.+ 17 Manja awo onse adzafooka ndipo mawondo awo onse azidzangochucha madzi.*+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani