Yeremiya 6:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Dulani mitengo kuti timange malo okwera oti timenyerepo nkhondo* ndi Yerusalemu.+ Yerusalemu ndi mzinda umene ukuyenera kuimbidwa mlandu.Mkati mwake muli kuponderezana kokhakokha.+ Yeremiya 32:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Taonani! Anthu abwera kumzinda uno ndipo amanga malo okwera omenyerapo nkhondo kuti aulande,+ moti uperekedwa mʼmanja mwa Akasidi amene akumenyana ndi anthu amumzindawu. Anthu adzafa ndi lupanga,+ njala ndi mliri.*+ Zinthu zonse zimene munanena zachitika ndipo ndi izi mukuzionazi.
6 Chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Dulani mitengo kuti timange malo okwera oti timenyerepo nkhondo* ndi Yerusalemu.+ Yerusalemu ndi mzinda umene ukuyenera kuimbidwa mlandu.Mkati mwake muli kuponderezana kokhakokha.+
24 Taonani! Anthu abwera kumzinda uno ndipo amanga malo okwera omenyerapo nkhondo kuti aulande,+ moti uperekedwa mʼmanja mwa Akasidi amene akumenyana ndi anthu amumzindawu. Anthu adzafa ndi lupanga,+ njala ndi mliri.*+ Zinthu zonse zimene munanena zachitika ndipo ndi izi mukuzionazi.